Dziwani
kuti
zomwe takhala tiri kufufuza poganiza kufunika kwache, koti tipeze mu CXR kuti
tithandauze kuchokera mumapapu odziwa bwino pantchito yawo, Erythrocyte
Sedimentation Rate (ESR), White Blood Cell Count (WBC) ndi Haemoglobin-level
(Hb) pamakhala zomwe zinapezeka m’makhololo zosatila zake kuti sanapezeke ndi chifuwa
chachikulu.
Malo
Zipatala
ziwiri za zing’ono zamuchigawo cha ku m’mwera kwa Malawi kwa amene ali ndi HIV
odwala TB ndi 80%.
Njira
Zomwe za retrospectively constructed cohort a chifuwa
cha chikulu , omwe anayezedwa makhololo, atalandi mankhwala koma, mankhwalawo
samathandize ai, atasatila pakutha mwezi 11.
Yankho
lomwe
Linapeze ka kwa anthu pagulu opanda chititezo cha
mthupi lawo omwe sali ndi chifuwa chachikulu mu CXR osika WBC ndi ESR wa
100-124 mm/hr chikana ochepa magazi low Hb pamezi itatu yokha, kunapezeka kuti
odwala chifuwa chachikulu. CXR ndi idwala omwe WBC inali yokwera.
zomwe tapeza odwala chifuwa
chachikulu chakwera kwambiri chifukwa cha HIV komanso omwe akuoneka kuti alibe
chitetezo chamatenda muthupi mwawo uko bvuta tikawayeza odwala makhololo ndi
CXR palimbe umboni weni weni woti akudwala chifuwa chachi kulu zosatila zake
sizimaoneka bwino ai ochilisa chibayo. Maka maka kwa modwala omwe amapezeka
kuti magazi awo a WBC nambala yake ndi yokwela kwambiri high WBC.